Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

d Kuwonongedwa kwa Babulo ndi chitsanzo chimodzi cha maulosi a m’Baibulo amene anakwaniritsidwa. Koma palinso zitsanzo zina monga za kuwonongedwa kwa mzinda wa Turo ndi Nineve. (Ezekieli 26:1-5; Zefaniya 2:13-15) Komanso ulosi wa Danieli unaneneratu kuti maulamuliro amphamvu a Mediya ndi Perisiya ndiponso Girisi ndi amene adzalamulire pambuyo pa ulamuliro wa Babulo. (Danieli 8:5-7, 20-22) Palinso maulosi ena ambiri onena za Mesiya omwe anakwaniritsidwa pa Yesu Khristu ndipo kuti mumve zambiri za maulosi amenewa, onani Zakumapeto tsamba 199-201.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena