Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Aisiraeli anatengera makhalidwe oipa a Akanani. Ponena za makhalidwe oipa a Akananiwo, womasulira Baibulo wina dzina lake Joseph Rotherham analemba kuti: “Akanani ankachita zinthu zonyansa komanso zankhanza kwambiri pa kulambira kwawo. Akazi ankalolera kuchita zinthu zoipa pofuna kulemekeza milungu yawo. M’malo awo opatulika ankachitiramo zachiwerewere. Analinso ndi zizindikiro ndi ziboliboli zonyansa zomwe zinkaimira maliseche. Komanso anthuwo anali ndi mahule opatulika, aamuna ndi aakazi.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena