Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Mwachitsanzo, pofunsa chifukwa chimene Myudayo ankalankhulira ndi Msamariya, mayiyo anayambitsa nkhani yokhudza chidani cha kalekale pakati pa anthu a mitundu iwiriyi. (Yohane 4:9) Iye ananenanso zoti Asamariya ndi mbadwa za Yakobo, mfundo imene Ayuda ankakanitsitsa kwa mtu wagalu. (Yohane 4:12) Ayuda ankawanena Asamariya kuti ndi Akuta, pofuna kutsindika mfundo yakuti iwo si mbadwa za Yakobo, koma ndi anthu amene anachokera kwa anthu a mitundu ina.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena