Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Pa nthawi ina mneneri Elisa anapereka malangizo ofanana ndi amenewa kwa Gehazi. Pamene ankatumiza mtumiki wakeyu kunyumba ya mayi wina amene mwana wake anamwalira, Elisa anamuuza kuti: “Ukakumana ndi munthu aliyense panjira usam’patse moni.” (2 Mafumu 4:29) Zimene anam’tumazo zinali zofunika kwambiri, choncho sanafunike kutaya nthawi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena