Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Yesu ataukitsidwa, anaonekera kwa “abale oposa 500.” (1 Akorinto 15:6) Popeza kuti pa nthawiyi otsatira ake ambiri anali ku Galileya, n’kutheka kuti imeneyi ndi nthawi yomwe yatchulidwa pa Mateyu 28:16-20. Choncho payenera kuti panali anthu ambiri pamene Yesu ankapereka lamulo loti otsatira akewo aziphunzitsa anthu kuti akhale ophunzira ake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena