Mawu a M'munsi
b Mtumwi Paulo yekha ndi amene ananena mawu amenewa omwe amapezeka pa Machitidwe 20:35. Zikuoneka kuti anachita kuuzidwa (ndi munthu wina amene anamva Yesu akulankhula kapena anawamva kwa Yesu ataukitsidwa) kapenanso anachita kuuziridwa ndi Mulungu.