Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Chaka chilichonse, Ayuda ankafunika kukhoma msonkho wa pakachisi wa ndalama zokwana madalakima awiri, ndipo ndalamazi zinkakwana pafupifupi malipiro a ntchito ya masiku awiri. Buku lina limati: “Ndalama za msonkhozi kwenikweni ankazigwiritsa ntchito polipirira zinthu zofunika popereka nsembe yopsereza imene inkaperekedwa tsiku ndi tsiku komanso nsembe zonse zimene ankaperekera anthu onse.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena