Mawu a M'munsi
b Mizimu yoipa ingathenso kumvera koma monyinyirika. Mwachitsanzo, pamene Yesu analamula kuti ziwanda zituluke mwa anthu ogwidwa ndi mizimu yoipayi, ziwandazo zinazindikira mphamvu imene Yesu anali nayo ndipo zinamumvera koma monyinyirika.—Maliko 1:27; 5:7-13.