Mawu a M'munsi
b Anthu ena okhulupirika akale ankakwatira mitala. Yehova analola anthu amenewa komanso mtundu wa Isiraeli kukwatira mitala. Yehova si amene anayambitsa mitala koma anapereka malamulo okhudza banja. Komabe, Akhristu amadziwa kuti masiku ano Yehova salolanso atumiki ake kukwatira mitala.—Mateyu 19:9; 1 Timoteyo 3:2.