Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Akatswiri a sayansi amanena kuti timakhala ndi luso lina lake limene limatithandiza kudziwa bwino thupi lathu komanso kudziwa pamene pali mikono ndi manja athu. Mwachitsanzo, luso limeneli limakuthandizani kuwomba m’manja ngakhale mutatsinzina. Munthu wina amene anadwala matenda owononga luso limeneli sankatha kuima, kuyenda ngakhalenso kukhala tsonga.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena