Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Katswiri wina ananena kuti pa nthawiyo panali lamulo la Kaisara limene linkaletsa munthu aliyense kulosera kuti “kudzabwera mfumu ina kapena ufumu, umene akuganiza kuti udzagonjetsa kapena kuweruza mfumu ya Roma imene inkalamulira pa nthawiyo.” Adani a Paulo ayenera kuti anapotoza uthenga wa mtumwiyu kuti aoneke ngati waphwanya lamulo limeneli. Onani bokosi lakuti “Olamulira a Roma M’nthawi ya Atumwi.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena