Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Patapita zaka zingapo, mtumwi Paulo analemba kalata yopita kwa Aheberi ndipo anasonyeza kuti pangano latsopano limaposa pangano lakale. M’kalatayo, iye anafotokoza momveka bwino kuti pangano latsopano linathetsa pangano lakale. Paulo anapereka mfundo zogwira mtima zimene Akhristu a Chiyuda akanagwiritsa ntchito poyankha Ayuda anzawo omwe ankaumirira Chilamulo cha Mose. Komanso mfundo zamphamvu zimene iye anafotokozazo ziyenera kuti zinalimbitsa chikhulupiriro cha Akhristu ena amene poyamba ankaumirirabe Chilamulo cha Mose.​—Aheb. 8:7-13.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena