Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Teritulo anayamikira Felike kuti anabweretsa “mtendere wambiri” m’dziko lawo. Koma zoona zake zinali zakuti pa nthawi imene Felike anali bwanamkubwa, ku Yudeya kunalibe mtendere poyerekezera ndi nthawi imene abwanamkubwa ena ankalamulira derali. Ndipo mtendere unapitirizabe kusokonekera mpaka pamene Ayuda anagalukira boma la Roma. Komanso iye ananama kwambiri ponena kuti Ayuda ‘ankayamikira kwambiri’ Felike chifukwa anasintha zinthu. Zoona zake zinali zakuti Ayuda ambiri ankadana naye chifukwa chowapondereza komanso chifukwa chopha mwankhanza Ayuda amene anaukira boma.​—Mac. 24:2, 3.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena