Mawu a M'munsi
a Chakumapeto kwa utumiki wa Yeremiya monga mneneri, kunalinso aneneri ena ngati: Habakuku, Obadiya, Danieli ndi Ezekieli. Pamene mzinda wa Yerusalemu unkawonongedwa mu 607 B.C.E., n’kuti Yeremiya atatumikira kwa zaka pafupifupi 40, ndipo anakhalabe ndi moyo zaka zoposa 20 mzindawu utawonongedwa.