Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Mawu achiheberi amene anawamasulira kuti “nsomba,” m’Chigiriki anawamasulira kuti “chilombo cha m’nyanja,” kapena kuti “chinsomba chachikulu.” Ngakhale kuti sitikudziwa kuti imeneyi inali nsomba yanji, komabe tikudziwa kuti m’nyanja ya Mediterranean muli nsomba zikuluzikulu zamtundu wa shaki zimene zingathe kumeza munthu wathunthu. M’nyanja zina nsomba zimenezi zimatha kukula kwambiri moti zina zimakhala zazitali mamita 15, kapenanso kuposa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena