Mawu a M'munsi
c Mfundo yakuti pa nthawiyi abusawa anali kuphiri ndi ziweto zawo ikutsimikizira zimene Baibulo limasonyeza, zoti Khristu sanabadwe m’mwezi wa December chifukwa pa nthawiyi ziweto sankapita nazo kutali. Choncho Khristu ayenera kuti anabadwa chakumayambiriro kwa October.