Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Kodi tikudziwa bwanji kuti Atate anaphunzitsa Mwana mmene angalalikirire? Taganizirani izi: Pophunzitsa, Yesu ankagwiritsa ntchito kwambiri mafanizo ndipo zimenezi zinakwaniritsa ulosi umene unalembedwa zaka zambirimbiri asanabadwe. (Sal. 78:2; Mat. 13:34, 35) Apa n’zoonekeratu kuti amene ananena ulosi umenewu, yemwe ndi Yehova, anadziwiratu kuti Mwana wake azidzaphunzitsa anthu pogwiritsa ntchito mafanizo kapena miyambi.​—2 Tim. 3:16, 17.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena