Mawu a M'munsi
f Masiku ano akulu onse amalowa mu Sukulu ya Utumiki wa Ufumu. Sukuluyi imachitika pakapita zaka zingapo ndipo nthawi imene imatenga imakhala yosiyanasiyana. Kuyambira m’chaka cha 1984 atumiki othandiza anayambanso kulowa nawo sukuluyi.