Mawu a M'munsi
a Anthu ena amaona kuti dzina lakuti Yehova limatanthauza kuti “Amachititsa Kukhala.” Tanthauzo limeneli likugwirizana ndi udindo wa Yehova monga Mlengi komanso Wokwaniritsa zolinga zake.
a Anthu ena amaona kuti dzina lakuti Yehova limatanthauza kuti “Amachititsa Kukhala.” Tanthauzo limeneli likugwirizana ndi udindo wa Yehova monga Mlengi komanso Wokwaniritsa zolinga zake.