Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Pofotokoza za mawu a Satanawa buku lina lofotokozera Baibulo linanena kuti: “Mofanana ndi mmene zinalili pa mayesero oyambirira amene Adamu ndi Hava analephera . . . , nkhani yagona pa kusankha pakati pa kuchita zimene Satana amafuna kapena kuchita zimene Mulungu amafuna, zomwe zikutanthauza kuti munthu akuyenera kusankha mmodzi woti azimulambira. Satana amafuna kuti anthu azimulambira m’malo molambira Mulungu yekha.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena