Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Zikuoneka kuti Mateyu anafotokoza mayeserowa potsatira ndondomeko ya mmene anachitikira, koma Luka analemba Uthenga Wabwino potsatira ndondomeko yosiyana ndi imeneyi. Tikutero chifukwa cha zifukwa zitatu zotsatirazi: (1) Pofotokoza mayesero achiwiri, Mateyu anayamba ndi mawu akuti “kenako,” kusonyeza kuti anali atafotokoza kale mayesero ena. (2) N’zomveka kunena kuti mayesero awiri osaonekerawo, amene akuyamba ndi mawu akuti, “Ngati ndinu mwana wa Mulungu,” akutsatana ndi mayesero oonekeratu ofuna kumuchititsa kuti aphwanye lamulo loyamba. (Eks. 20:2, 3) (3) Komanso n’zomveka kunena kuti mawu a Yesu akuti “Choka Satana!” anawanena pambuyo pa mayesero achitatu komanso omaliza.​—Mat. 4:5, 10, 11.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena