Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Zikuoneka kuti Abele anabadwa patangopita nthawi yochepa Adamu ndi Hava atathamangitsidwa m’munda wa Edeni. (Gen. 4:1, 2) Lemba la Genesis 4:25 limanena kuti Mulungu anapereka Seti “mʼmalo mwa Abele.” Adamu anali ndi zaka 130 pamene anabereka Seti, pambuyo poti Abele waphedwa mwankhanza. (Gen. 5:3) Choncho Abele ayenera kuti anali ndi zaka 100 pamene Kaini anamupha.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena