Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Pogwiritsa ntchito mawu akuti “nsanje” Yehova anasonyeza kuti amaona kuti nkhani yokhala okhulupirika kwa iye ndi yaikulu. Zikutipangitsa kuganiza za mkwiyo umene mwamuna amakhala nawo chifukwa cha nsanje mkazi wake akachita zinthu zosakhulupirika. (Miy. 6:34) Mofanana ndi mwamuna ameneyu, Yehova anakwiyiranso anthu amene anachita nawo pangano atayamba kulambira mafano. Buku lina linanena kuti: “Mulungu amachita nsanje . . . chifukwa choti ndi woyera. Popeza kuti iye yekha ndi Woyera . . . , Safuna kuti wina aliyense azipikisana naye.”​—Eks. 34:14.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena