Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a N’zomveka kunena kuti Ezekieli anachita zizindikiro zonsezi anthu akuonerera. N’chifukwa chiyani tikutero? Chifukwa chakuti pamene anamuuza kuti achite zinthu zina ngati kuphika chakudya komanso kunyamula katundu, Yehova analamula Ezekieli kuti achite zinthu zimenezi “iwo akuona.”​—Ezek. 4:12; 12:7.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena