Mawu a M'munsi
a Mwachitsanzo, Afilisiti analetsa kuti pasapezeke aliyense wosula zitsulo mu Isiraeli. Aisiraeli ankayenera kupita kwa Afilisiti kuti akawanolere zipangizo zawo zolimira ndipo ankawalipiritsa ndalama zimene munthu ankalandira akagwira ntchito masiku ambiri.—1 Sam. 13:19-22.