Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Mafupa amene Ezekieli anaona m’masomphenyawo sanali a anthu amene anafa chifukwa cha matenda koma a ‘anthu amene anachita kuphedwa.’ (Ezek. 37:9) “Nyumba yonse ya Isiraeli” inaphedwadi mophiphiritsa pamene anthu okhala mu ufumu wa mafuko 10 wa Isiraeli komanso anthu okhala mu ufumu wa mafuko awiri wa Yuda anagonjetsedwa ndi Asuri komanso Ababulo n’kutengedwa kupita ku ukapolo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena