Mawu a M'munsi
b Masomphenya a kachisi amene Ezekieli anaona, akugwirizananso ndi maulosi ena okhudza kubwezeretsedwa kwa kulambira koyera amene akukwaniritsidwa m’masiku otsiriza ano. Mwachitsanzo, onani kufanana komwe kulipo pakati pa Ezekieli 43:1-9 ndi Malaki 3:1-5 komanso Ezekieli 47:1-12 ndi Yoweli 3:18.