Mawu a M'munsi
b Malinga ndi zimene buku lina limanena, mawu a Chiheberi amene anawamasulira kuti “cholakwa” angatanthauze zinthu “zoipa kwambiri.” Buku lina limanena kuti mawu amenewa “akukhudzana kwambiri ndi zachipembedzo ndipo pafupifupi nthawi zonse amasonyeza kuti munthu ali ndi mlandu pamaso pa Mulungu chifukwa cha makhalidwe ake oipa.”