Mawu a M'munsi
c Lemba la Danieli 11:45 limasonyeza kuti mfumu yakumpoto idzaukira anthu a Mulungu chifukwa limanena kuti: “Mfumuyo idzamanga matenti achifumu pakati pa nyanja yaikulu [Mediterranean] ndi phiri lopatulika la Dziko Lokongola [kumene poyamba kunali kachisi wa Mulungu komanso kumene anthu ankalambirira].”