Mawu a M'munsi
c Mofanana ndi zimenezi, ganizirani fanizo la Yesu la khoka. Khoka limagwira nsomba zambiri koma si zonse zimene zimakhala “zabwino.” Nsomba zoipazo amangozitaya. Choncho Yesu anachenjeza kuti anthu ena amene alowa m’gulu la Yehova, pakapita nthawi, akhoza kusonyeza kuti ndi osakhulupirika.—Mat. 13:47-50; 2 Tim. 2:20, 21.