Mawu a M'munsi
b M’Clintock ndi Strong amawalongosola iwo kukhala “amodzi a mipatuko yakale kwambiri ndi yotchuka kwenikweni ya sunagoge wa Ayuda, amene chizindikiro chawo chowasiyanitsa ndicho kumamatira kwawo gwagwagwa kumawu onse olembedwa achilamulo.”