Mawu a M'munsi
c “Iwo amapha nyama madzulo . . . Pakati pausiku banja lirilonse limadya nyamayo . . . ndiyeno kutentha nyama yotsalayo ndi mafupa ake kusanache . . . Akatswiri ena apereka lingaliro lakuti chipembedzo cha Asamariya chingafanane kwenikweni ndi chipembedzo chabaibulo Chiyuda cha arabi chisanachisinthe.”—The Origins of the Seder.