Mawu a M'munsi
a “Anomia kuli kunyalanyaza, kapena kuchitira mwano, malamulo a Mulungu; asebeia [mpangidwe wa nauni wa liwu lotembenuzidwa ‘anthu opanda umulungu’] uli mkhalidwe umodzimodziwo kulinga ku Munthu wa Mulungu.”—Vine’s Expository Dictionary of Old and New Testament Words, Volyumu 4, tsamba 170.