Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Onse aŵiri The Encyclopedia Americana ndi Great Soviet Encyclopedia amavomerezana kuti kulamulira kwa Aritasasta kunatha mu 424 B.C.E. Kodi kunayamba liti? Mu 474 B.C.E. Kuchilikiza ichi, malembo ozokotedwa ofukulidwa pansi ena ali ndi madeti a chaka cha 50 cha Aritasasta; ena amasonyeza kuti iye analowedwa mmalo m’chaka chake cha 51. Titapenda chafutambuyo zaka zokwanira 50 kuchokera mu 424 B.C.E., timapeza 474 B.C.E. kukhala deti limene iye anayamba kulamulira kwake. Chotero, chaka chokwanitsa 20 cha Aritasasta, pamene lamulo lija linaperekedwa, chikakhala zaka zokwanira 19 m’kulamulira kwake, ndiko kuti, mu 455 B.C.E. Kaamba ka tsatanetsatane wowonjezereka, onani Insight on the Scriptures, Volyumu 2, tsamba 616, yofalitsidwa ndi Watchtower Bible and Tract Society of New York, Inc.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena