Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Liwu Lachigiriki logwiritsiridwa ntchito panopa, an·tiʹly·tron, silimapezeka kwina kulikonse m’Baibulo. Ilo nlogwirizana ndi liwu limene Yesu analigwiritsira ntchito kutanthauza dipo (lyʹtron) pa Marko 10:45. Komabe, The New International Dictionary of New Testament Theology imanena kuti an·tiʹly·tron ‘limapereka lingaliro la kusinthanitsa.’ Moyenerera, New World Translation imalimasulira kukhala “dipo lolinganira.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena