Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Yerekezerani njira ziŵiri zimene Paulo anachitira pankhani ya mdulidwe. Ngakhale kuti anadziŵa kuti “mdulidwe ulibe kanthu,” anamdula mnzake woyenda naye Timoteo, amene anali Myuda kumbali ya amake. (1 Akorinto 7:19; Machitidwe 16:3) M’nkhani ya Tito, mtumwi Paulo anapeŵa kumdula chifukwa cholimbana ndi Ayuda. (Agalatiya 2:3) Tito anali Mgiriki ndipo chotero, mosiyana ndi Timoteo, analibe chifukwa chenicheni chodulidwira. Ngati iye, Wamitundu, akanati adulidwe, ‘Kristu sakanapindula naye kanthu.’​—Agalatiya 5:2-4.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena