Mawu a M'munsi
a Kalelo mu 1864 wodziŵa zaumulungu R. Govett anakulongosola motere: “Zimenezi zikuwonekera kukhala zotsimikizirika kwambiri. Kuperekedwa kwa chizindikiro cha Kukhalapo kumasonyeza kuti nkwachinsinsi. Sitifunikira chizindikiro kuti tidziwe kukhalapo kwa zimene tikuwona.”