Mawu a M'munsi
b Pali makiliniki ambiri, zipatala, ndi njira zina zochiritsira zimene zingathandize. Nsanja ya Olonda siikukusankhirani chithandizo chilichonse. Munthu ayenera kusamala kuti asadziloŵetse m’machitachita amene akalolera molakwa malamulo amkhalidwe a Baibulo. Komabe, potsirizira pake, aliyense ayenera kudzisankhira yekha mtundu wa chithandizo chofunikira.