Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Josephus analemba za zochitika pakati pa kuukira Yerusalemu koyamba kwa Aroma (66 C.E.) ndi chiwonongeko chake kuti: “Usikuwo kunaulika mkuntho wowononga; namondwe anawomba, mvula yamkokomo inagwa, mphezi zinang’anima mosalekeza, mabingu anagunda mochititsa mantha, dziko linanjenjemera ndi phokoso logonthetsa m’khutu. Tsoka la mtundu wa anthu linasonyezedweratu ndi kunyonyotsoka kwa mpangidwe wonse wa zinthu kumeneku, ndipo palibe aliyense amene anakayikira kuti zizindikirozi zinasonyeza tsoka lopanda lina lofanana nalo.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena