Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

d Chimene Yesu anatcha “masauko aakulu” ndi “chisautso” chinali kuwonongedwa kwa dongosolo Lachiyuda, monga tanthauzo lake loyamba. Koma m’mavesi amene ali ndi tanthauzo la m’tsiku lathu lokha, m’malemba oyambirira, anagwiritsira ntchito phatikizo lotsimikizira lakuti “cho,” akumati “chisautso chachikulucho.” (Mateyu 24:21, 29; Marko 13:19, 24) Lemba la Chivumbulutso 7:14 linatcha chochitika cha mtsogolo chimenechi “chisautso chachikulu,” kwenikweni “chisautso chachikulucho.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena