Mawu a M'munsi
a Zimenezi zingakhale zovuta kwa Akristu amene amalemba pepala la msonkho limodzi ndi mnzawo wa muukwati wosakhulupirira. Mkazi Wachikristu adzayesayesa kwambiri kukhala wachikatikati pa kusunga lamulo la umutu ndi kumvera malamulo a msonkho a Kaisara. Komabe, ayenera kuzindikira zotulukapo za lamulo za kusaina pepala limene akudziŵa kuti nlonama.—Yerekezerani ndi Aroma 13:1; 1 Akorinto 11:3.