Mawu a M'munsi
b Chokondweretsa nchakuti, Uthenga Wabwino wa Mateyu ndiwo wokha umene umasimba za chochitika chimenechi m’moyo wa Yesu padziko lapansi. Pokhala wokhometsa msonkho wakale, mosakayikira Mateyu anachita chidwi kwambiri ndi mzimu wa Yesu pankhani imeneyi.