Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Pamene kuli kwakuti Baibulo limanena kuti “chimene munthu achifesa, chimenenso adzachituta,” zimenezi sizimatanthauza kuti kuvutika kwa munthu kuli chilango cha Mulungu. (Agalatiya 6:7) M’dziko lolamulidwa ndi Satanali, kaŵirikaŵiri olungama amavutika kwambiri kuposa mmene amachitira oipa. (1 Yohane 5:19) “Adzada inu anthu onse chifukwa cha dzina langa,” Yesu anauza motero ophunzira ake. (Mateyu 10:22) Matenda ndi mitundu ina ya tsoka zingagwere atumiki a Mulungu okhulupirika alionse.​—Salmo 41:3; 73:3-5; Afilipi 2:25-27.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena