Mawu a M'munsi
a Mkulu angasankhe kuŵerenga nkhani za mu Nsanja ya Olonda ndi Galamukani! ndi anthu otero—mwachitsanzo, nkhani yakuti “Kodi Mudzapindula ndi Chisomo?” ndi “Kupambana Nkhondo Yolimbana ndi Kuchita Tondovi.”—Nsanja ya Olonda ya February 15 ndi March 1, 1990.