Mawu a M'munsi
a M’malo ena kungafunikire kugwiritsira ntchito mawu osinthidwa a lumbiroli kuti ligwirizane ndi malamulo akumaloko. (Mateyu 22:21) Komabe, m’maiko ochuluka okwatirana achikristu ochuluka amagwiritsira ntchito lumbiro limene lili pamwambapa.