Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Afarisi kwenikweni ndiwo anali ndi thayo la kuyambitsa mtundu wa Chiyuda chimene chiliko lerolino, chotero nkosadabwitsa kuti Chiyuda chimafunabe njira zozembera ziletso zake za Sabata zambiri zowonjezedwa. Mwachitsanzo, mlendo ku chipatala cha Ayuda amwambo pa Sabata angapeze kuti chikepe chimaima chokha pamalo alionse kuti okweramo asachite “ntchito” yauchimo ya kusinika batani ya chikepe. Madokotala ena achiyuda amalemba mapepala otengerapo mankhwala ndi inki imene imazimirira pambuyo pa masiku angapo. Chifukwa ninji? Mishnah imati kulemba ndi “ntchito,” koma imamasulira kuti “kulemba” ndiko kusiya chilembo chachikhalire.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena