Mawu a M'munsi
b Kemosi ndiye anali mulungu wamkulu wa Amoabu. (Numeri 21:29; Yeremiya 48:46) Pazochitika zina, ana ayenera kuti anaperekedwa nsembe kwa mulungu wonyansa ndi wonyenga ameneyu.—2 Mafumu 3:26, 27.
b Kemosi ndiye anali mulungu wamkulu wa Amoabu. (Numeri 21:29; Yeremiya 48:46) Pazochitika zina, ana ayenera kuti anaperekedwa nsembe kwa mulungu wonyansa ndi wonyenga ameneyu.—2 Mafumu 3:26, 27.