Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Yesu analimba mtima poukira eni malonda aphindu amenewo. Malinga ndi wolemba mbiri wina, panali kobiri lakale lachiyuda limene linafunika polipira msonkho wa pakachisi. Chotero alendo ambiri omwe anafika pakachisi anayenera kusintha ndalama zawo kuti alipire msonkho. Osinthitsa ndalama anali ndi ufulu wokhazikitsa mtengo wachikhalire wosinthira ndalama, motero iwo anapindula ndalama zambiri.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena