Mawu a M'munsi
a Yesu analimba mtima poukira eni malonda aphindu amenewo. Malinga ndi wolemba mbiri wina, panali kobiri lakale lachiyuda limene linafunika polipira msonkho wa pakachisi. Chotero alendo ambiri omwe anafika pakachisi anayenera kusintha ndalama zawo kuti alipire msonkho. Osinthitsa ndalama anali ndi ufulu wokhazikitsa mtengo wachikhalire wosinthira ndalama, motero iwo anapindula ndalama zambiri.