Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Kagulu kawo kanachokera kwa Ahasidi, gulu limene linakhalako zaka mazana ambiri kalelo kutsekereza chisonkhezero cha Agiriki. Ahasidi anatenga dzina lawo ku liwu lachihebri lakuti chasi·dhimʹ, kapena kuti “okhulupirika.” Mwina iwo ankaganiza kuti malemba omwe amatchula “okhulupirika” a Yehova anali kunena makamaka za iwo. (Salmo 50:5, NW) Iwowo, ndi Afarisi omwe anawatsatira, anadziika okha kutetezera zilembo za Chilamulo ndipo kukangalika kwawo kunali konkitsa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena