Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Kalikonse ka tindalama timeneti kanali ka lepton, ndalama yaing’ono koposa yachiyuda imene inali kugwiritsiridwa ntchito nthaŵi imeneyo. Ma lepton aŵiri anali ofanana ndi gawo limodzi mwa magawo 64 a malipiro a tsiku limodzi. Malinga nkunena kwa Mateyu 10:29, ndi kobiri la assarion (lofanana ndi ma lepton asanu ndi atatu), munthu anali kugula mpheta ziŵiri, zimene zinali zina mwa mbalame zotsika mtengo kwambiri zimene osauka anali kudya. Choncho, mkazi wamasiye ameneyu analidi wosauka, chifukwa chakuti anali ndi theka la ndalama yogulira mpheta imodzi, yosakwanira nkomwe kudyera chakudya.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena